YouVersion Logo
Search Icon

ZEKARIYA Mau Oyamba

Mau Oyamba
Bukuli lili ndi zigawo ziwiri: Gawo loyamba ndi mau amene mneneri adalalikira kuyambira chaka cha 520 BC. Zekariya akulongosola zimene adaziwona m'masomphenya ndipo akuwachenjeza anthuwo nawalimbitsa mtima kuti akonzenso Kachisi komanso mzinda wa Yerusalemu. Iwo ayenera adziyeretsa popeza Yehova adzawadalitsa (1—8). Gawo lachiwiri ndi kaundula wa mauneneri osiyanasiyana onena za kubwera kwa Mesiya ndipo tsiku la chiweruzo (9—14).
Za mkatimu
Mau oyamba 1.1—8.23
Mau a Yehova aimba mlandu mitundu ina ya anthu 9.1-8
Mau ena olonjeza zabwino 9.9—14.21

Highlight

Share

Copy

None

Want to have your highlights saved across all your devices? Sign up or sign in