1
MASALIMO 84:11
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Pakuti Yehova Mulungu ndiye dzuwa ndi chikopa; Yehova adzapatsa chifundo ndi ulemerero; sadzakaniza chokoma iwo akuyenda angwiro.
Compare
Explore MASALIMO 84:11
2
MASALIMO 84:10
Pakuti tsiku limodzi m'mabwalo anu likoma koposa masiku ambirimbiri akukhala pena. Kukhala ine wapakhomo m'nyumba ya Mulungu wanga, kundikonda ine koposa kugonera m'mahema a choipa.
Explore MASALIMO 84:10
3
MASALIMO 84:5
Wodala munthu amene mphamvu yake ili mwa Inu; mumtima mwake muli makwalala a ku Ziyoni.
Explore MASALIMO 84:5
4
MASALIMO 84:2
Moyo wanga ulakalaka, inde ukomokanso ndi kufuna mabwalo a Yehova; mtima wanga ndi thupi langa zifuulira kwa Mulungu wamoyo.
Explore MASALIMO 84:2
Home
Bible
Plans
Videos