1
YEREMIYA 15:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Mau anu anapezeka, ndipo ndinawadya; mau anu anakhala kwa ine chikondwero ndi chisangalalo cha mtima wanga; pakuti ndatchedwa dzina lanu, Yehova Mulungu wa makamu.
Compare
Explore YEREMIYA 15:16
2
YEREMIYA 15:19
Chifukwa chake atero Yehova, Ukabwerera pamenepo ndidzakubwezanso, kuti uime pamaso panga; ndipo ukasiyanitsa cha mtengo wake ndi chonyansa, udzakhala ngati m'kamwa mwanga; ndipo adzabwerera kwa iwe, koma sudzabwerera kwa iwo.
Explore YEREMIYA 15:19
3
YEREMIYA 15:21
Ndipo ndidzakulanditsa iwe m'dzanja la oipa, ndipo ndidzakuombola iwe m'dzanja la oopsa.
Explore YEREMIYA 15:21
Home
Bible
Plans
Videos