1
YEREMIYA 16:21
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Chifukwa chake, taonani, ndidzadziwitsa iwo kamodzi aka, ndidzawadziwitsa dzanja langa ndi mphamvu yanga; ndipo adzadziwa kuti dzina langa ndine Yehova.
Compare
Explore YEREMIYA 16:21
2
YEREMIYA 16:19
Inu Yehova, mphamvu yanga, ndi linga langa, pothawirapo panga tsiku la msauko, amitundu adzadza kwa Inu kuchokera ku malekezero a dziko lapansi, ndipo adzati, Makolo athu analandira cholowa cha bodza lokha, zopanda pake ndi zinthu zosapindula nazo.
Explore YEREMIYA 16:19
3
YEREMIYA 16:20
Kodi munthu adzadzipangira yekha milungu, imene siili milungu?
Explore YEREMIYA 16:20
Home
Bible
Plans
Videos