1
HOSEYA 8:7
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Pakuti abzala mphepo, nadzakolola kamvulumvulu; alibe tirigu wosasenga; ngala siidzatulutsa ufa; chinkana iutulutsa, alendo adzaumeza.
Compare
Explore HOSEYA 8:7
2
HOSEYA 8:4
Analonga mafumu, koma sikunachokera kwa Ine; anaika akalonga, koma sindinadziwa; anadzipangira mafano a siliva wao ndi golide wao, kuti akalikhidwe.
Explore HOSEYA 8:4
Home
Bible
Plans
Videos