1
HOSEYA 9:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Mulungu wanga adzawataya, pakuti sanammvere Iye; ndipo adzakhala othawathawa mwa amitundu.
Compare
Explore HOSEYA 9:17
2
HOSEYA 9:1
Usakondwera, Israele, ndi kusekerera, ngati mitundu ya anthu; pakuti wachita chigololo kuleka Mulungu wako, wakonda mphotho ya chigololo pa dwale la tirigu lililonse.
Explore HOSEYA 9:1
3
HOSEYA 9:7
Masiku a kulanga afika, masiku a kubwezera afika; Israele adzadziwa; mneneri ali wopusa, munthu wamzimu ali wamisala, chifukwa cha kuchuluka mphulupulu yako, ndi popeza udani ndi waukulu.
Explore HOSEYA 9:7
Home
Bible
Plans
Videos