1
HOSEYA 7:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo sanafuulire kwa Ine ndi mtima wao, koma alira pakama pao, asonkhanira tirigu ndi vinyo, apikisana ndi Ine.
Compare
Explore HOSEYA 7:14
2
HOSEYA 7:13
Tsoka kwa iwowa! Pakuti anandizembera; chionongeko kwa iwowa! Pakuti anandilakwira; ndikadawalanditsa Ine, koma anandinenera zabodza.
Explore HOSEYA 7:13
Home
Bible
Plans
Videos