1
HOSEYA 6:6
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Pakuti ndikondwera nacho chifundo, si nsembe ai; ndi kumdziwa Mulungu kuposa nsembe zopsereza.
Compare
Explore HOSEYA 6:6
2
HOSEYA 6:3
Tidziwe tsono, tilondole kudziwa Yehova; kutuluka kwake kwakonzekeratu ngati matanda kucha; ndipo adzatidzera ngati mvula, ngati mvula ya masika yakuthirira dziko.
Explore HOSEYA 6:3
3
HOSEYA 6:1
Tiyeni, tibwerere kunka kwa Yehova; pakuti wang'amba, nadzatipoletsera; wakantha, nadzatimanga.
Explore HOSEYA 6:1
Home
Bible
Plans
Videos