1
HOSEYA 5:15
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndidzamuka ndi kubwerera kunka kumalo kwanga, mpaka adzavomereza kupalamula kwao, nafunafuna nkhope yanga; m'msauko mwao adzandifunafuna mwachangu.
Compare
Explore HOSEYA 5:15
2
HOSEYA 5:4
Machitidwe ao sawalola kubwerera kwa Mulungu wao; pakuti mzimu wa uhule uli m'kati mwao, ndipo sadziwa Yehova.
Explore HOSEYA 5:4
Home
Bible
Plans
Videos