1
HOSEYA 4:6
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Anthu anga aonongeka chifukwa cha kusadziwa; popeza unakana kudziwa, Inenso ndikukaniza, kuti usakhale wansembe wanga; popeza waiwala chilamulo cha Mulungu wako, Inenso ndidzaiwala ana ako.
Compare
Explore HOSEYA 4:6
2
HOSEYA 4:1
Imvani mau a Yehova, inu ana a Israele; pakuti Yehova ali ndi mlandu ndi okhala m'dziko, popeza palibe choonadi, kapena chifundo, kapena kudziwa Mulungu m'dziko.
Explore HOSEYA 4:1
Home
Bible
Plans
Videos