1
HOSEYA 3:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo Yehova anati kwa ine, Mukanso, konda mkazi wokondedwa ndi bwenzi lake, koma wakuchita chigololo, monga Yehova akonda ana a Israele, angakhale atembenukira kumilungu ina, nakonda nchinchi za mphesa zouma.
Compare
Explore HOSEYA 3:1
2
HOSEYA 3:5
atatero ana a Israele adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wake masiku otsiriza.
Explore HOSEYA 3:5
Home
Bible
Plans
Videos