1
HOSEYA 2:19-20
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo ndidzakutomera ukhale wanga kosatha, inde ndidzakutomera ukhale wanga m'chilungamo, ndi m'chiweruzo, ndi m'ukoma mtima, ndi m'chifundo. Ndidzakutomeranso ukhale wanga mokhulupirika, ndipo udzadziwa Yehova.
Compare
Explore HOSEYA 2:19-20
2
HOSEYA 2:15
Ndipo ndidzampatsa minda yake yamphesa kuyambira pomwepo, ndi chigwa cha Akori chikhale khomo la chiyembekezo; ndipo adzavomereza pomwepo monga masiku a ubwana wake, ndi monga tsiku lokwera iye kutuluka m'dziko la Ejipito.
Explore HOSEYA 2:15
Home
Bible
Plans
Videos