Yoh. 3:16

Yoh. 3:16 BLY-DC

Mulungutu adaŵakonda kwambiri anthu a pa dziko lonse lapansi. Anali naye Mwana mmodzi yekha, komabe adampereka kuti aliyense wokhulupirira Iyeyo asatayike, koma akhale ndi moyo wosatha.

Прочитати Yoh. 3

Пов'язані відео