1
Gen. 34:25
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Patangopita masiku atatu, zilonda za kuumbala kuja zisanapole pa anthu aja, ana aŵiri a Yakobe, Simeoni ndi Levi, alongo ake a Dina, adatenga mikondo yao, nakaloŵa mosadziŵika mumzinda muja, nkukapha amuna onse.
Compare
Explore Gen. 34:25
Home
Bible
Plans
Videos