1
Gen. 29:20
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Motero Yakobe adagwira ntchito zaka zisanu ndi ziŵiri kuti akwatire Rakele, ndipo nthaŵi imeneyo idangooneka kwa iye ngati masiku oŵerengeka chabe, chifukwa choti adaamkonda kwambiri mkaziyo.
Compare
Explore Gen. 29:20
2
Gen. 29:31
Chauta ataona kuti Yakobe sankakonda kwambiri Leya, adalola kuti Leyayo abale ana, koma Rakele ai.
Explore Gen. 29:31
Home
Bible
Plans
Videos