1
Gen. 30:22
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Tsono Mulungu adakumbukira Rakele, namva pemphero lake, nkulola kuti abale ana.
Compare
Explore Gen. 30:22
2
Gen. 30:24
Motero mwanayo adamutcha Yosefe, nanena kuti, “Mulungu andipatse wina mwana.”
Explore Gen. 30:24
3
Gen. 30:23
Iyenso adatenga pathupi, nabala mwana wamwamuna. Ndipo adati, “Mulungu wandichotsa manyazi a uchumba wanga.”
Explore Gen. 30:23
Home
Bible
Plans
Videos