1
MIKA 5:2
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Koma iwe, Betelehemu Efurata, ndiwe wamng'ono kuti ukhale mwa zikwi za Yuda, mwa iwe mudzanditulukira wina wakudzakhala woweruza m'Israele; matulukiro ake ndiwo a kale lomwe, kuyambira nthawi yosayamba.
Compare
Explore MIKA 5:2
2
MIKA 5:4
Ndipo adzaimirira, nadzadyetsa nkhosa zake mu mphamvu ya Yehova, m'ukulu wa dzina la Yehova Mulungu wake; ndipo iwo adzakhalabe; pakuti pamenepo Iye adzakhala wamkulu kufikira malekezero a dziko lapansi.
Explore MIKA 5:4
Home
Bible
Plans
Videos