1
MIKA 6:8
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Iye anakuuza, munthuwe, chomwe chili chokoma; ndipo Yehova afunanji nawe koma kuti uchite cholungama, ndi kukonda chifundo ndi kuyenda modzichepetsa ndi Mulungu wako.
Compare
Explore MIKA 6:8
2
MIKA 6:4
Pakuti ndinakukwezani kukutulutsani m'dziko la Ejipito, ndi kuombola inu m'nyumba ya ukapolo; ndipo ndinatuma akutsogolereni Mose, Aroni, ndi Miriyamu.
Explore MIKA 6:4
Home
Bible
Plans
Videos