1
YAKOBO 2:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Momwemonso chikhulupiriro, chikapanda kukhala nacho ntchito, chikhala chakufa m'kati mwakemo.
Compare
Explore YAKOBO 2:17
2
YAKOBO 2:26
Pakuti monga thupi lopanda mzimu lili lakufa, koteronso chikhulupiriro chopanda ntchito chili chakufa.
Explore YAKOBO 2:26
3
YAKOBO 2:14
Chipindulo chake nchiyani, abale anga, munthu akanena, Ndili nacho chikhulupiriro, koma alibe ntchito? Kodi chikhulupirirocho chikhoza kumpulumutsa?
Explore YAKOBO 2:14
4
YAKOBO 2:19
Ukhulupirira iwe kuti Mulungu ali mmodzi; uchita bwino; ziwanda zikhulupiriranso, ndipo zinthunthumira.
Explore YAKOBO 2:19
5
YAKOBO 2:18
Koma wina akati, Iwe uli nacho chikhulupiriro, ndipo ine ndili nazo ntchito; undionetse ine chikhulupiriro chako chopanda ntchito zako, ndipo ine ndidzakuonetsa iwe chikhulupiriro changa chotuluka m'ntchito zanga.
Explore YAKOBO 2:18
6
YAKOBO 2:13
Pakuti chiweruziro chilibe chifundo kwa iye amene sanachita chifundo; chifundo chidzitamandira kutsutsana nacho chiweruziro.
Explore YAKOBO 2:13
7
YAKOBO 2:24
Mupenya kuti munthu ayesedwa wolungama ndi ntchito yake, osati ndi chikhulupiriro chokha.
Explore YAKOBO 2:24
8
YAKOBO 2:22
Upenya kuti chikhulupiriro chidachita pamodzi ndi ntchito zake, ndipo motuluka mwa ntchito chikhulupiriro chidayesedwa changwiro
Explore YAKOBO 2:22
Home
Bible
Plans
Videos