1
YESAYA 8:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Yehova wa makamu, Iye mudzamyeretsa; muope Iye, akuchititseni mantha Iye.
Compare
Explore YESAYA 8:13
2
YESAYA 8:12
Musachinene, Chiwembu; chilichonse chimene anthu awa adzachinena, Chiwembu; musaope monga kuopa kwao kapena musachite mantha.
Explore YESAYA 8:12
3
YESAYA 8:20
Kuchilamulo ndi kuumboni! Ngati iwo sanena malinga ndi mau awa, ndithu sadzaona mbandakucha.
Explore YESAYA 8:20
Home
Bible
Plans
Videos