1
YESAYA 7:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Chifukwa chake Ambuye mwini yekha adzakupatsani inu chizindikiro; taonani namwali adzaima, nadzabala mwana wamwamuna, nadzamutcha dzina lake Imanuele.
Compare
Explore YESAYA 7:14
2
YESAYA 7:9
ndipo mutu wa Efuremu ndi Samariya, ndi mutu wa Samariya ndi mwana wa Remaliya, mukapanda kukhulupirira ndithu simudzakhazikika.
Explore YESAYA 7:9
3
YESAYA 7:15
Iye adzadya mafuta ndi uchi, pamene adziwa kukana choipa ndi kusankha chabwino.
Explore YESAYA 7:15
Home
Bible
Plans
Videos