1
EZARA 3:11
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo anathirirana mang'ombe, kulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi kuti, Pakuti ndiye wabwino, pakuti chifundo chake nchosalekeza pa Israele. Nafuula anthu onse ndi chimfuu chachikulu, pomlemekeza Yehova; popeza adamanga maziko a nyumba ya Yehova.
Compare
Explore EZARA 3:11
2
EZARA 3:12
Koma ansembe ambiri, ndi Alevi, ndi akulu a nyumba za makolo, okalamba amene adaona nyumba yoyamba ija, pomanga maziko a nyumba iyi pamaso pao, analira ndi mau akulu; koma ambiri anafuulitsa mokondwera.
Explore EZARA 3:12
Home
Bible
Plans
Videos