1
EZEKIELE 8:3
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo anatambasula chonga dzanja, nandigwira tsitsi la pamutu panga; ndipo mzimu unandilengetsa pakati pa dziko ndi thambo, numuka nane m'masomphenya a Mulungu ku Yerusalemu, ku chitseko cha chipata cha bwalo la m'katimo loloza kumpoto, kumene kunali mpando wa fano la nsanje lochititsa nsanje.
Compare
Explore EZEKIELE 8:3
2
EZEKIELE 8:12
Pamenepo anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, wapenya kodi chochita akulu a nyumba ya Israele mumdima, aliyense m'chipinda chake cha zifanizo? Pakuti ati, Yehova satipenya, Yehova wataya dziko.
Explore EZEKIELE 8:12
3
EZEKIELE 8:18
Chifukwa chake Inenso ndidzachita mwaukali; diso langa silidzalekerera, osawachitira chifundo Ine; ndipo chinkana afuula m'makutu mwanga ndi mau akulu, koma sindidzawamvera Ine.
Explore EZEKIELE 8:18
Home
Bible
Plans
Videos