1
AMOSI 4:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Pakuti taona, Iye amene aumba mapiri, nalenga mphepo, nafotokozera munthu maganizo ake, nasanduliza m'mawa ukhale mdima, naponda pa misanje ya dziko lapansi, dzina lake ndiye Yehova Mulungu wa makamu.
Compare
Explore AMOSI 4:13
2
AMOSI 4:12
Chifukwa chake ndidzatero nawe, Israele; popeza ndidzakuchitira ichi, dzikonzeretu kukomana ndi Mulungu wako, Israele.
Explore AMOSI 4:12
3
AMOSI 4:6
Ndipo Ine ndakupatsaninso mano oyera m'midzi yanu yonse, ndi kusowa mkate m'malo mwanu monse; koma simunabwerera kudza kwa Ine, ati Yehova.
Explore AMOSI 4:6
Home
Bible
Plans
Videos