1
1 PETRO 5:7
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
ndi kutaya pa Iye nkhawa yanu yonse, pakuti Iye asamalira inu.
Compare
Explore 1 PETRO 5:7
2
1 PETRO 5:10
Ndipo Mulungu wa chisomo chonse, amene adakuitanani kulowa ulemerero wake wosatha mwa Khristu, mutamva zowawa kanthawi, adzafikitsa inu opanda chilema mwini wake, adzakhazikitsa, adzalimbikitsa inu.
Explore 1 PETRO 5:10
3
1 PETRO 5:8-9
Khalani odzisungira, dikirani; mdani wanu mdierekezi, monga mkango wobuma, ayendayenda ndi kufunafuna wina akamlikwire: ameneyo mumkanize okhazikika m'chikhulupiriro, podziwa kuti zowawa zomwezo zilimkukwaniridwa pa abale anu ali m'dziko.
Explore 1 PETRO 5:8-9
4
1 PETRO 5:6
Potero dzichepetseni pansi pa dzanja la mphamvu la Mulungu, kuti panthawi yake akakukwezeni
Explore 1 PETRO 5:6
5
1 PETRO 5:5
Momwemonso, anyamata inu, mverani akulu. Koma nonsenu muvale kudzichepetsa kuti mutumikirane; pakuti Mulungu akaniza odzikuza, koma apatsa chisomo kwa odzichepetsa.
Explore 1 PETRO 5:5
Home
Bible
Plans
Videos