1
1 YOHANE 3:18
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Tiana, tisakonde ndi mau, kapena ndi lilime, komatu ndi kuchita ndi m'choonadi.
Compare
Explore 1 YOHANE 3:18
2
1 YOHANE 3:16
Umo tizindikira chikondi, popeza Iyeyu anapereka moyo wake chifukwa cha ife; ndipo ife tiyenera kupereka moyo wathu chifukwa cha abale.
Explore 1 YOHANE 3:16
3
1 YOHANE 3:1
Taonani, chikondicho Atate watipatsa, kuti titchedwe ana a Mulungu; ndipo tili ife otere. Mwa ichi dziko lapansi silizindikira ife, popeza silimzindikira Iye.
Explore 1 YOHANE 3:1
4
1 YOHANE 3:8
iye wochita tchimo ali wochokera mwa mdierekezi, chifukwa mdierekezi amachimwa kuyambira pachiyambi. Kukachita ichi Mwana wa Mulungu adaonekera, ndiko kuti akaononge ntchito za mdierekezi.
Explore 1 YOHANE 3:8
5
1 YOHANE 3:9
Yense wobadwa kuchokera mwa Mulungu sachita tchimo, chifukwa mbeu yake ikhala mwa iye; ndipo sakhoza kuchimwa, popeza wabadwa kuchokera mwa Mulungu.
Explore 1 YOHANE 3:9
6
1 YOHANE 3:17
Koma iye amene ali nacho chuma cha dziko lapansi, naona mbale wake ali wosowa ndi kutsekereza chifundo chake pommana iye, nanga chikondi cha Mulungu chikhala mwa iye bwanji?
Explore 1 YOHANE 3:17
7
1 YOHANE 3:24
Ndipo munthu amene asunga malamulo ake akhala mwa Iye, ndi Iye mwa munthuyo. Ndipo m'menemo tizindikira kuti akhala mwa ife, kuchokera mwa Mzimu amene anatipatsa ife.
Explore 1 YOHANE 3:24
8
1 YOHANE 3:10
M'menemo aoneka ana a Mulungu, ndi ana a mdierekezi: yense wosachita chilungamo siali wochokera mwa Mulungu; ndi iye wosakonda mbale wake.
Explore 1 YOHANE 3:10
9
1 YOHANE 3:11
Pakuti uwu ndi uthenga mudaumva kuyambira pachiyambi, kuti tikondane wina ndi mnzake
Explore 1 YOHANE 3:11
10
1 YOHANE 3:13
Musazizwe, abale, likadana nanu dziko lapansi.
Explore 1 YOHANE 3:13
Home
Bible
Plans
Videos