1
2 Akorinto 11:14-15
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Sizododometsa zimenezi, pakuti Satana mwini amadzizimbayitsa kuoneka ngati mngelo wowunikira anthu. Nʼzosadabwitsa tsono ngati atumiki ake akudzizimbayitsa ngati otumikira chilungamo. Matsiriziro awo adzalandira zoyenerana ndi ntchito zawo.
Compare
Explore 2 Akorinto 11:14-15
2
2 Akorinto 11:3
Koma ndikuopa kuti monga Hava ananyengedwa ndi kuchenjera kwa njoka, mitima yanunso ingasocheretsedwe kuleka nʼkudzipereka moona mtima ndi modzipereka kwenikweni kwa Khristu.
Explore 2 Akorinto 11:3
3
2 Akorinto 11:30
Ngati nʼkoyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira pa zinthu zimene zimaonetsa kufowoka kwanga.
Explore 2 Akorinto 11:30
Home
Bible
Plans
Videos