1
2 Akorinto 10:5
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Timagonjetsa maganizo onse onyenga ndiponso kudzikuza kulikonse kolimbana ndi anthu kuti asadziwe Mulungu. Ndipo timagonjetsa ganizo lililonse kuti limvere Khristu.
Compare
Explore 2 Akorinto 10:5
2
2 Akorinto 10:4
Pakuti zida zathu zankhondo si zida za dziko lapansi. Koma ndi mphamvu zochokera kwa Mulungu zotha kugwetsa malinga.
Explore 2 Akorinto 10:4
3
2 Akorinto 10:3
Ngakhale ife timakhala mʼdziko lapansi, sitimenya nkhondo monga mmene dziko lapansi limachitira.
Explore 2 Akorinto 10:3
4
2 Akorinto 10:18
Pakuti munthu amene amavomerezedwa, si amene amadziyenereza yekha, koma munthu amene Ambuye amuyenereza.
Explore 2 Akorinto 10:18
Home
Bible
Plans
Videos