1
YOHANE 18:36
Buku Lopatulika
Yesu anayankha, Ufumu wanga suli wa dziko lino lapansi; ufumu wanga ukadakhala wa dziko lino lapansi, anyamata anga akadalimbika nkhondo, kuti ndisaperekedwe kwa Ayuda; koma tsopano ufumu wanga suli wochokera konkuno.
Qhathanisa
Hlola YOHANE 18:36
2
YOHANE 18:11
Pamenepo Yesu anati kwa Petro, Longa lupanga m'chimake chake; chikho chimene Atate wandipatsa Ine sindimwere ichi kodi?
Hlola YOHANE 18:11
Ikhaya
IBhayibheli
Amapulani
Amavidiyo