1
YOHANE 3:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi kotero, kuti anapatsa Mwana wake wobadwa yekha, kuti yense wakhulupirira Iye asatayike, koma akhale nao moyo wosatha.
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí YOHANE 3:16
2
YOHANE 3:17
Pakuti Mulungu sanatume Mwana wake kudziko lapansi, kuti akaweruze dziko lapansi, koma kuti dziko lapansi likapulumutsidwe ndi Iye.
Ṣàwárí YOHANE 3:17
3
YOHANE 3:3
Yesu anayankha nati kwa iye, Indetu, indetu, ndinena ndi iwe, Ngati munthu sabadwa mwatsopano, sakhoza kuona Ufumu wa Mulungu.
Ṣàwárí YOHANE 3:3
4
YOHANE 3:18
Wokhulupirira Iye saweruzidwa; wosakhulupirira waweruzidwa ngakhale tsopano, chifukwa sanakhulupirire dzina la Mwana wobadwa yekha wa Mulungu.
Ṣàwárí YOHANE 3:18
5
YOHANE 3:19
Koma chiweruziro ndi ichi, kuti kuunika kunadza kudziko lapansi, ndipo anthu anakonda mdima koposa kuunika; pakuti ntchito zao zinali zoipa.
Ṣàwárí YOHANE 3:19
6
YOHANE 3:30
Iyeyo ayenera kukula koma ine ndichepe.
Ṣàwárí YOHANE 3:30
7
YOHANE 3:20
Pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika, ndipo sakudza kwa kuunika, kuti zingatsutsidwe ntchito zake.
Ṣàwárí YOHANE 3:20
8
YOHANE 3:36
Iye amene akhulupirira Mwanayo ali nao moyo wosatha; koma iye amene sakhulupirira Mwanayo sadzaona moyo, koma mkwiyo wa Mulungu ukhala pa iye.
Ṣàwárí YOHANE 3:36
9
YOHANE 3:14
Ndipo monga Mose anakweza njoka m'chipululu, chotero Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa
Ṣàwárí YOHANE 3:14
10
YOHANE 3:35
Atate akonda Mwana, nampatsa zinthu zonse m'dzanja lake.
Ṣàwárí YOHANE 3:35
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò