1
Genesis 13:15
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Dziko lonse ukulionalo ndidzalipereka kwa iwe ndi zidzukulu zako mpaka muyaya.
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Genesis 13:15
2
Genesis 13:14
Loti atachoka, Yehova anati kwa Abramu, “Kuchokera pamene ulipo tayangʼanayangʼana cha kumpoto, kummwera, kummawa ndi kumadzulo.
Ṣàwárí Genesis 13:14
3
Genesis 13:16
Ndidzakupatsa zidzukulu zochuluka ngati fumbi lapansi moti amene angathe kuwerenga fumbilo ndiye kuti angathenso kuwerenga zidzukulu zako.
Ṣàwárí Genesis 13:16
4
Genesis 13:8
Tsono Abramu anati kwa Loti, “Pasakhale mikangano pakati pa iwe ndi ine kapena pakati pa abusa ako ndi anga, popeza ndife abale.
Ṣàwárí Genesis 13:8
5
Genesis 13:18
Choncho Abramu anasamutsa tenti yake napita kukakhala pafupi ndi mitengo ikuluikulu ija ya thundu ya ku Mamre ku Hebroni, kumene anamangira Yehova guwa lansembe.
Ṣàwárí Genesis 13:18
6
Genesis 13:10
Loti atamwazamwaza maso anaona kuti chigwa chonse cha mtsinje wa Yorodani chinali chothiriridwa bwino ngati munda wa Yehova, kapena ngati dziko la ku Igupto mpaka ku Zowari. (Nthawi iyi nʼkuti Yehova asanawononge Sodomu ndi Gomora).
Ṣàwárí Genesis 13:10
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò