Логотип YouVersion
БібліяПланиВідео
Завантажити додаток
Вибір мови
Іконка пошуку

Популярні біблійні вірші з YOHANE 9

1

YOHANE 9:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.

Порівняти

Дослідити YOHANE 9:4

2

YOHANE 9:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.

Порівняти

Дослідити YOHANE 9:5

3

YOHANE 9:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.

Порівняти

Дослідити YOHANE 9:2-3

4

YOHANE 9:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.

Порівняти

Дослідити YOHANE 9:39

Безплатні плани читання та молитовні роздуми до YOHANE 9

Попередній розділ
Наступний розділ
YouVersion

Заохочуємо та закликаємо вас шукати близькості з Богом щодня.

Служіння

Про YouVersion

Кар'єра

Стати волонтером

Блоґ

Преса

Корисні посилання

Допомога

Пожертвувати

Біблійні видання

Аудіо Біблії

Мови Біблії

Вірш дня


Цифрове служіння

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Політика конфіденційностіУмови
Програма виявлення вразливостей
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Головна

Біблія

Плани

Відео