1
Yohane 9:4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Ife tiyenera kugwira ntchito za Iye amene anandituma kukanali masana. Usiku ukubwera, pamene wina aliyense sadzagwira ntchito.
Karşılaştır
Yohane 9:4 keşfedin
2
Yohane 9:5
Pamene Ine ndili mʼdziko lapansi, Ine ndine kuwunika kwa dziko lapansi.”
Yohane 9:5 keşfedin
3
Yohane 9:2-3
Ophunzira ake anamufunsa Iye kuti, “Rabi anachimwa ndani, munthuyu kapena makolo ake, kuti iye abadwe wosaona?” Yesu anayankha kuti, “Sikuti iyeyu anachimwa kapena makolo ake, koma izi zinachitika kuti Mulungu aonetse ntchito zake mwa iyeyu.
Yohane 9:2-3 keşfedin
4
Yohane 9:39
Yesu anati, “Ndinabwera pansi pano kudzaweruza kuti osaona aone ndi openya asaone.”
Yohane 9:39 keşfedin
Ana Sayfa
Kutsal Kitap
Okuma Planları
Videolar