Ntc. 25:8
Ntc. 25:8 BLY-DC
Paulo poyankha zomnenezazo adati, “Ine sindidalakwirepo Malamulo a Ayuda, kapena Nyumba ya Mulungu, kapenanso Mfumu ya ku Roma.”
Paulo poyankha zomnenezazo adati, “Ine sindidalakwirepo Malamulo a Ayuda, kapena Nyumba ya Mulungu, kapenanso Mfumu ya ku Roma.”