Logo ng YouVersion
Hanapin ang Icon

Ntc. 15:8-9

Ntc. 15:8-9 BLY-DC

Ndipo Mulungu amene amadziŵa mitima ya anthu, adaŵachitira umboni pakuŵapatsa Mzimu Woyera, monga adapatsira ifeyo. Mulungu sadasiyanitse konse pakati pa ife ndi iwo, koma adayetsera mitima yao ndi chikhulupiriro chao.