1
Ntc. 6:3-4
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Nchifukwa chake abale, pakati panupa sankhanipo amuna asanu ndi aŵiri, a mbiri yabwino, odzazidwa ndi Mzimu Woyera ndiponso ndi nzeru. Tidzapatsa iwowo ntchitoyi. Koma ife tidzadzipereka ku ntchito ya kupemphera ndi kulalika mau a Mulungu.”
Paghambingin
I-explore Ntc. 6:3-4
2
Ntc. 6:7
Mau a Mulungu ankafalikira ponseponse, ndipo ophunzira ankachulukirachulukira ndithu ku Yerusalemu. Ansembe omwe ambirimbiri ankamvera chikhulupirirocho.
I-explore Ntc. 6:7
Home
Biblia
Mga Gabay
Mga Palabas