1
Ntc. 19:6
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Pamene Paulo adaŵasanjika manja, Mzimu Woyera adadza pa iwo, ndipo adayamba kulankhula zilankhulo zosadziŵika, ndi kumalalika mau ochokera kwa Mulungu.
Paghambingin
I-explore Ntc. 19:6
2
Ntc. 19:11-12
Mulungu adachita zozizwitsa kwambiri kudzera kwa Paulo. Anthu ankati akatenga zitambaya kapena nsalu zina zimene Paulo ankagwiritsa ntchito, nakaziika pa anthu odwala, odwalawo ankachira, ndipo mizimu yoipa inkatuluka mwa iwo.
I-explore Ntc. 19:11-12
3
Ntc. 19:15
Koma mzimu woipawo udayankha kuti, “Yesu ndimamdziŵa, Paulonso ndimamdziŵa, koma inuyo ndinu yani?”
I-explore Ntc. 19:15
Home
Biblia
Mga Gabay
Mga Palabas