1
Gen. 37:5
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Tsiku lina Yosefe adalota maloto, nafotokozera abale ake malotowo. Zitatero, adadana naye kopambana kale.
เปรียบเทียบ
สำรวจ Gen. 37:5
2
Gen. 37:3
Israele ankakonda Yosefe kupambana ana ake ena onse, popeza kuti anali mwana wake wapaukalamba. Adamsokera mkanjo wautali wamanja.
สำรวจ Gen. 37:3
3
Gen. 37:4
Abale ake ataona kuti bambo wao ankakonda Yosefe kupambana iwowo, adayamba kudana naye Yosefeyo, ndipo sankalankhula naye mokondwa.
สำรวจ Gen. 37:4
4
Gen. 37:9
Tsono Yosefe adalotanso ena maloto, nauzanso abale akewo kuti, “Ndalotanso, ndipo ndaona dzuŵa, mwezi ndi nyenyezi khumi ndi imodzi zikundiŵeramira.”
สำรวจ Gen. 37:9
5
Gen. 37:11
Tsono abale ake aja adachita naye kaduka kwambiri. Koma atate ake ankakhala akuziganiza zimenezi.
สำรวจ Gen. 37:11
6
Gen. 37:6-7
Iye adaŵauza kuti “Mverani maloto omwe ndalota. Tonsefe tinali m'munda, ndipo tinalikumanga mitolo yatirigu. Tilikumanga chomwecho, mtolo wanga unaimirira. Tsono mitolo yanu inauzungulira mtolo wangawo ndi kumauŵeramira.”
สำรวจ Gen. 37:6-7
7
Gen. 37:20
Tiyeni timuphe, mtembo wake tiwuponye m'chitsime china mwa zitsime zili apazi. Tizikanena kuti wajiwa ndi chilombo, ndipo tidzaone tanthauzo lake la maloto ake aja.”
สำรวจ Gen. 37:20
8
Gen. 37:28
Tsono Amidiyani ena amalonda adafika pomwepo. Abale akewo adamtulutsa Yosefeyo m'chitsime muja, namgulitsa kwa Aismaelewo pamtengo wokwana masekeli a siliva makumi aŵiri, ndipo iwowo adapita naye ku Ejipito.
สำรวจ Gen. 37:28
9
Gen. 37:19
Onsewo ankauzana kuti, “Uyotu kamaloto uja, akudza apoyo!
สำรวจ Gen. 37:19
10
Gen. 37:18
Abale ake aja adamuwonera kutali, iye asanayandikire nkomwe pamene panali iwopo. Adayamba kumpangira chiwembu natsimikiza zoti amuphe.
สำรวจ Gen. 37:18
11
Gen. 37:22
Tingomuponya m'chitsime chopanda madzichi kuchipululu konkuno. Tisampweteke konse.” Ankanena zimenezi akuganiza zomupulumutsa m'manja mwao, kuti amtumize kwa bambo wake.
สำรวจ Gen. 37:22
หน้าหลัก
พระคัมภีร์
แผนการอ่านต่างๆ
วิดีโอ