1
Gen. 29:20
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Motero Yakobe adagwira ntchito zaka zisanu ndi ziŵiri kuti akwatire Rakele, ndipo nthaŵi imeneyo idangooneka kwa iye ngati masiku oŵerengeka chabe, chifukwa choti adaamkonda kwambiri mkaziyo.
เปรียบเทียบ
สำรวจ Gen. 29:20
2
Gen. 29:31
Chauta ataona kuti Yakobe sankakonda kwambiri Leya, adalola kuti Leyayo abale ana, koma Rakele ai.
สำรวจ Gen. 29:31
หน้าหลัก
พระคัมภีร์
แผนการอ่านต่างๆ
วิดีโอ