1
Marko 15:34
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Pa ora lachisanu ndi chinayi Yesu analira mofuwula kuti, “Eloi, Eloi, lama sabakitani?” Kutanthauza kuti, “Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?”
ஒப்பீடு
Marko 15:34 ஆராயுங்கள்
2
Marko 15:39
Ndipo Kenturiyo, amene anayima patsogolo pa Yesu, atamva kulira kwake ndi kuona mmene anafera anati, “Zoonadi, uyu anali Mwana wa Mulungu.”
Marko 15:39 ஆராயுங்கள்
3
Marko 15:38
Chinsalu chotchinga cha mʼNyumba ya Mulungu chinangʼambika pakati kuyambira pamwamba mpaka pansi.
Marko 15:38 ஆராயுங்கள்
4
Marko 15:37
Ndi mawu ofuwula, Yesu anapuma komaliza.
Marko 15:37 ஆராயுங்கள்
5
Marko 15:33
Pa ora lachisanu ndi chimodzi masana mdima unabwera pa dziko lonse mpaka pa ora lachisanu ndi chinayi masana.
Marko 15:33 ஆராயுங்கள்
6
Marko 15:15
Pilato pofuna kuwakondweretsa anthuwo, anawamasulira Baraba. Analamula kuti Yesu akwapulidwe mwankhanza, ndipo anamupereka kuti akapachikidwe.
Marko 15:15 ஆராயுங்கள்
முகப்பு
வேதாகமம்
வாசிப்புத் திட்டங்கள்
காணொளிகள்