Logo YouVersion
Ikona Hľadať

YOHANE 13:34-35

YOHANE 13:34-35 BLPB2014

Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake. Mwa ichi adzazindikira onse kuti muli ophunzira anga, ngati muli nacho chikondano wina ndi mnzake.

Video pre YOHANE 13:34-35

Bezplatné plány čítania a zamyslenia týkajúce sa YOHANE 13:34-35