1
YOHANE 3:16
Buku Lopatulika
Pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi kotero, kuti anapatsa Mwana wake wobadwa yekha, kuti yense wakukhulupirira Iye asatayike, koma akhale nao moyo wosatha.
සසඳන්න
YOHANE 3:16 ගවේෂණය කරන්න
2
YOHANE 3:17
Pakuti Mulungu sanatume Mwana wake kudziko lapansi, kuti akaweruze dziko lapansi, koma kuti dziko lapansi likapulumutsidwe ndi Iye.
YOHANE 3:17 ගවේෂණය කරන්න
3
YOHANE 3:3
Yesu anayankha nati kwa iye, Indetu, indetu, ndinena ndi iwe, Ngati munthu sabadwa mwatsopano, sangathe kuona Ufumu wa Mulungu.
YOHANE 3:3 ගවේෂණය කරන්න
4
YOHANE 3:18
Wokhulupirira Iye saweruzidwa; wosakhulupirira waweruzidwa ngakhale tsopano, chifukwa sanakhulupirire dzina la Mwana wobadwa yekha wa Mulungu.
YOHANE 3:18 ගවේෂණය කරන්න
5
YOHANE 3:19
Koma chiweruziro ndi ichi, kuti kuunika kunadza kudziko lapansi, ndipo anthu anakonda mdima koposa kuunika; pakuti ntchito zao zinali zoipa.
YOHANE 3:19 ගවේෂණය කරන්න
6
YOHANE 3:30
Iyeyo ayenera kukula koma ine ndichepe.
YOHANE 3:30 ගවේෂණය කරන්න
7
YOHANE 3:20
Pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika, ndipo sakudza kwa kuunika, kuti zingatsutsidwe ntchito zake.
YOHANE 3:20 ගවේෂණය කරන්න
8
YOHANE 3:36
Iye amene akhulupirira Mwanayo ali nao moyo wosatha; koma iye amene sakhulupirira Mwanayo sadzaona moyo, koma mkwiyo wa Mulungu ukhala pa iye.
YOHANE 3:36 ගවේෂණය කරන්න
9
YOHANE 3:14
Ndipo monga Mose anakweza njoka m'chipululu, chotero Mwana wa Munthu ayenera kukwezedwa
YOHANE 3:14 ගවේෂණය කරන්න
10
YOHANE 3:35
Atate akonda Mwana, nampatsa zinthu zonse m'dzanja lake.
YOHANE 3:35 ගවේෂණය කරන්න
නිවස
බයිබලය
සැලසුම්
වීඩියෝ