Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z GENESIS 2

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 2:24

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 2:18

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 2:7

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 2:23

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 2:3

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

Porównaj

Przeglądaj GENESIS 2:25

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: GENESIS 2

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Strona główna

Biblia

Plany

Nagrania wideo