1
Gen. 2:24
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.
ႏွိုင္းယွဥ္
Gen. 2:24ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
Gen. 2:18
Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”
Gen. 2:18ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
Gen. 2:7
Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.
Gen. 2:7ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
Gen. 2:23
Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”
Gen. 2:23ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
5
Gen. 2:3
Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.
Gen. 2:3ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
6
Gen. 2:25
Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.
Gen. 2:25ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
YouVersion သည္ မိမိအေတြ႕အၾကဳံကို စိတ္ႀကိဳက္ျပင္ဆင္ရန္ ကြတ္ကီးမ်ားကို အသုံးျပဳသည္။ ကၽြန္ုပ္တို႔၏ဝဘ္ဆိုဒ္ကိုအသုံးျပဳျခင္းျဖင့္ ကၽြန္ုပ္တို႔၏ ကိုယ္ေရးကိုယ္တာမူဝါဒတြင္ေဖာ္ျပထားသည့္အတိုင္း ကၽြန္ုပ္တို႔၏ cookies အသုံးျပဳမွုကို လက္ခံပါသည္။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား