1
LUKA 12:40
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Khalani okonzeka inunso; chifukwa nthawi imene simulingirira, Mwana wa Munthu akudza.
ႏွိုင္းယွဥ္
LUKA 12:40ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
LUKA 12:31
Komatu tafunafunani Ufumu wake, ndipo izi adzakuonjezerani.
LUKA 12:31ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
LUKA 12:15
Ndipo Iye anati kwa iwo, Yang'anirani, mudzisungire kupewa msiriro uliwonse; chifukwa moyo wake wa munthu sulingana ndi kuchuluka kwa zinthu zake ali nazo.
LUKA 12:15ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
LUKA 12:34
Pakuti kumene kuli chuma chanu, komweko kudzakhalanso mtima wanu.
LUKA 12:34ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
5
LUKA 12:25
Ndipo ndani wa inu, ndi kuda nkhawa angathe kuonjeza mkono pa msinkhu wake?
LUKA 12:25ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
6
LUKA 12:22
Ndipo Iye anati kwa ophunzira ake, Chifukwa chake ndinena ndinu, Musade nkhawa ndi moyo wanu, chimene mudzadya; kapena ndi thupi lanu, chimene mudzavala.
LUKA 12:22ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
7
LUKA 12:7
komatu ngakhale matsitsi onse a pamutu panu awerengedwa. Musaopa, muposa mtengo wake wa mpheta zambiri.
LUKA 12:7ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
8
LUKA 12:32
Musaopa, kagulu ka nkhosa inu; chifukwa Atate wanu akonda kukupatsani Ufumu.
LUKA 12:32ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
9
LUKA 12:24
Lingirirani makungubwi, kuti samafesai, kapena kutemai; alibe nyumba yosungiramo, kapena nkhokwe; ndipo Mulungu awadyetsa; nanga inu simuziposa mbalame kwambiri!
LUKA 12:24ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
10
LUKA 12:29
Ndipo inu musafunefune chimene mudzadya, ndi chimene mudzamwa; ndipo musakayike mtima.
LUKA 12:29ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
11
LUKA 12:28
Koma ngati Mulungu aveka kotere udzu wa kuthengo ukhala lero, ndipo mawa uponyedwa pamoto; nanga inu sadzakuninkhani koposa, inu okhulupirira pang'ono?
LUKA 12:28ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
12
LUKA 12:2
Koma kulibe kanthu kovundikiridwa kamene sikadzaululidwa; ndi kobisika kamene sikadzadziwika.
LUKA 12:2ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား