1
GENESIS 29:20
Buku Lopatulika
Ndipo Yakobo anamtumikira zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele; koma zidamuonekera iye ngati masiku owerengeka chifukwa cha chikondi chimene anamkonda iye nacho.
ႏွိုင္းယွဥ္
GENESIS 29:20ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
GENESIS 29:31
Pamene Yehova anaona kuti anamuda Leya, anatsegula m'mimba mwake; koma Rakele anali wouma.
GENESIS 29:31ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
က်မ္းစာ
အစီအစဥ္
ဗီဒီယို