1
Gen. 2:24
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.
비교
Gen. 2:24 살펴보기
2
Gen. 2:18
Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”
Gen. 2:18 살펴보기
3
Gen. 2:7
Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.
Gen. 2:7 살펴보기
4
Gen. 2:23
Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”
Gen. 2:23 살펴보기
5
Gen. 2:3
Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.
Gen. 2:3 살펴보기
6
Gen. 2:25
Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.
Gen. 2:25 살펴보기
홈
성경
묵상
동영상