YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

GENESIS 2 - 인기 성경 구절

1

GENESIS 2:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.

비교

GENESIS 2:24 살펴보기

2

GENESIS 2:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yehova Mulungu ndipo anati, Si kwabwino kuti munthu akhale yekha; ndidzampangira womthangatira iye.

비교

GENESIS 2:18 살펴보기

3

GENESIS 2:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova Mulungu anaumba munthu ndi dothi lapansi, nauzira mpweya wa moyo m'mphuno mwake; munthuyo nakhala wamoyo.

비교

GENESIS 2:7 살펴보기

4

GENESIS 2:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Adamu, Uyu tsopano ndiye fupa la mafupa anga, ndi mnofu wa mnofu wanga; ndipo adzatchedwa Mkazi, chifukwa anamtenga mwa mwamuna.

비교

GENESIS 2:23 살펴보기

5

GENESIS 2:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Mulungu ndipo anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri, naliyeretsa limenelo: chifukwa limenelo adapuma ku ntchito yake yonse imene Mulungu anailenga ndi kupanga.

비교

GENESIS 2:3 살펴보기

6

GENESIS 2:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Onse awiri ndipo anali amaliseche, mwamuna ndi mkazi wake, ndipo analibe manyazi.

비교

GENESIS 2:25 살펴보기

GENESIS 2: 관련 무료 묵상 계획

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상