1
GENESIS 10:8
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
Ndipo Kusi anabala Nimirodi; ndipo iye anayamba kukhala wamphamvu pa dziko lapansi.
비교
GENESIS 10:8 살펴보기
2
GENESIS 10:9
Iye ndiye mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova: chifukwa chake kunanenedwa, Monga Nimirodi mpalu wamphamvu pamaso pa Yehova.
GENESIS 10:9 살펴보기
홈
성경
묵상
동영상