YouVersion 로고
성경묵상동영상
앱 다운로드
언어 선택
검색 아이콘

GENESIS 13 - 인기 성경 구절

1

GENESIS 13:15

Buku Lopatulika

BLP-2018

chifukwa kuti dziko lonse limene ulinkuona, ndidzakupatsa iwe ndi mbeu yako nthawi yonse.

비교

GENESIS 13:15 살펴보기

2

GENESIS 13:14

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, atalekana naye Loti, Tukulatu maso ako, nuyang'anire kuyambira kumene uliko, kumpoto, ndi kumwera, ndi kum'mawa, ndi kumadzulo

비교

GENESIS 13:14 살펴보기

3

GENESIS 13:16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ndidzayesa mbeu yako monga fumbi lapansi: chotere kuti ngati munthu angathe kuwerenga fumbi lapansi, chomwechonso mbeu yako idzawerengedwa.

비교

GENESIS 13:16 살펴보기

4

GENESIS 13:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Abramu anati kwa Loti, Tisachite ndeu, ine ndi iwe, abusa anga ndi abusa ako: chifukwa kuti ife ndife abale.

비교

GENESIS 13:8 살펴보기

5

GENESIS 13:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Abramu anasuntha hema wake nafika nakhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure, imene ili mu Hebroni, nammangira Yehova kumeneko guwa la nsembe.

비교

GENESIS 13:18 살펴보기

6

GENESIS 13:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Loti anatukula maso ake nayang'ana chigwa chonse cha Yordani kuti chonsecho chinali ndi madzi ambiri, asanaononge Yehova Sodomu ndi Gomora, monga munda wa Yehova, monga dziko la Ejipito pakunka ku Zowari.

비교

GENESIS 13:10 살펴보기

이전 장
다음 장
YouVersion

매일 하나님과 친밀하게 동행하도록 격려하고 도전하기.

사역

소개

채용 정보

자원 봉사

블로그

기사

유용한 링크

도움

후원

성경 번역본

오디오 성경

성경 언어

오늘의 말씀


디지털 사역

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

개인 정보 취급 정책약관
취약점 공개 프로그램
페이스북트위터인스타그램유튜브핀터레스트

홈

성경

묵상

동영상